Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 40:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Asilikali onse a gulu la Yuda amene analembedwa mayina alipo 186,400. Amenewa azikhala oyamba kunyamuka.+

  • Numeri 2:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Asilikali onse a gulu la Rubeni amene analembedwa mayina alipo 151,450. Amenewa azikhala achiwiri kunyamuka.+

      17 Posamutsa chihema chokumanako,+ gulu la Alevi lizikhala pakati pa magulu enawo.

      Dongosolo limene azitsatira posamuka,+ ndi limenenso azitsatira pomanga misasa yawo, aliyense pamalo ake, mogwirizana ndi gulu lawo la mafuko atatu.

  • Numeri 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Asilikali onse a gulu la Efuraimu amene anawalemba mayina alipo 108,100. Amenewa azikhala achitatu kunyamuka.+

  • Numeri 2:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Asilikali onse a gulu la Dani amene analembedwa mayina alipo 157,600. Amenewa azikhala omalizira kunyamuka,+ mogwirizana ndi magulu a Aisiraeli a mafuko atatuatatu.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani