Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 17:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 78:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anangʼamba miyala mʼchipululu,

      Anawalola kumwa madziwo mpaka ludzu kutha ngati kuti akumwa madzi amʼnyanja.+

  • Salimo 105:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 114:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amene amasintha thanthwe kukhala dambo la madzi,

      Komanso mwala wa nsangalabwi kukhala akasupe a madzi.+

  • Yesaya 48:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo sanamve ludzu pamene iye ankawatsogolera kudutsa mʼchipululu.+

      Iye anachititsa kuti madzi atuluke pathanthwe kuti iwo amwe.

      Anangʼamba thanthwe nʼkupangitsa kuti madzi atuluke.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani