Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Oweruza 11:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mafumu 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pa nthawiyi mʼpamene Solomo anamangira Kemosi malo okwezeka.+ Kemosi anali mulungu wonyansa wa Amowabu ndipo anamʼmangira malowo paphiri lomwe linali pafupi ndi Yerusalemu. Anamangiranso Moleki,+ mulungu wonyansa wa Aamoni,+ malo okwezeka.

  • 2 Mafumu 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Komanso inachititsa kuti malo okwezeka akutsogolo kwa Yerusalemu omwe anali kumʼmwera* kwa Phiri Lachiwonongeko,* amene Solomo mfumu ya Isiraeli inamangira Asitoreti mulungu wamkazi wonyansa wa Asidoni, Kemosi mulungu wonyansa wa Amowabu ndi Milikomu+ mulungu wonyansa wa Aamoni,+ akhale osayenera kulambirako.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani