Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 22:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno buluyo ataona mngelo wa Yehova ataima pamsewu lupanga lake lili mʼmanja, anayesa kuchoka mumsewu nʼkupatukira kutchire. Koma Balamu anayamba kumʼkwapula kuti abwerere mumsewu.

  • Numeri 22:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Buluyo ataonanso mngelo wa Yehova uja, anayamba kudzikanikizira kukhoma, moti anakanikiziranso phazi la Balamu kukhomako. Ndipo Balamu anayamba kumʼkwapulanso buluyo.

  • Numeri 22:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Buluyo ataonanso mngelo wa Yehova uja, anangokhala pansi, Balamu ali pamsana pake. Choncho Balamu anapsa mtima koopsa, ndipo anapitiriza kumukwapula ndi ndodo yake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani