Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 23:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno Balamu anauza Balaki kuti: “Mukhale pompano pafupi ndi nsembe yanu yopsereza ndipo ine ndichoka. Mwina Yehova alankhula nane ndipo zimene andiuzezo ndikuuzani.” Choncho Balamu anapita pamwamba pa phiri.

  • Numeri 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 23:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Palibe amene angalodze Yakobo,+

      Kapena kuombeza maula polimbana ndi Isiraeli.+

      Panopa anthu anganene zokhudza Yakobo kapena kuti Isiraeli kuti:

      ‘Taonani zimene Mulungu wachita!’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani