-
Numeri 22:10, 11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Balamu anayankha Mulungu woonayo kuti: “Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu ndi amene watumiza anthuwa kuti adzandiuze kuti, 11 ‘Taonani! Anthu amene achokera ku Iguputo aja adzaza dziko lonse lapansi kumene munthu angayangʼane. Tsopano bwerani, mudzatemberere anthuwa.+ Mwina ndingathe kumenyana nawo nʼkuwathamangitsa.’”
-