Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 1:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Uike Alevi kuti aziyangʼanira chihema cha Umboni+ ndi ziwiya zake zonse komanso chilichonse cha mmenemo.+ Iwowo ndi amene azinyamula chihemacho ndi ziwiya zake zonse.+ Ndi amenenso azitumikira pachihemapo+ ndipo azimanga misasa yawo mozungulira chihemacho.+

  • Numeri 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Aroni azipereka Aleviwo kwa Yehova monga nsembe yoyendetsa uku ndi uku+ yochokera kwa Aisiraeli ndipo iwo azigwira ntchito yotumikira Yehova.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani