-
Yesaya 26:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Chifukwa taonani! Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala
Kuti adzaimbe mlandu anthu okhala mʼdzikoli chifukwa cha zolakwa zawo,
Ndipo dzikoli lidzaonetsa poyera magazi amene linakhetsa
Ndipo silidzabisanso anthu ake amene anaphedwa.”
-
-
Yeremiya 26:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Koma mudziwe kuti mukandipha, inuyo, mzindawu ndi anthu onse amene akukhala mumzindawu mukhala ndi mlandu wa magazi chifukwa chopha munthu wosalakwa. Ndithudi, Yehova ndi amene wandituma kuti ndidzakuuzeni mawu onse amene mwamvawa.”
-