Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Maliro 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Maso anga atopa ndi kugwetsa misozi.+

      Mʼmimba mwanga mukubwadamuka.

      Chiwindi changa chakhuthulidwa pansi chifukwa cha kuwonongedwa kwa mwana wamkazi wa anthu anga,+

      Ndiponso chifukwa chakuti ana ndi makanda akukomoka mʼmabwalo a mzinda.+

  • Maliro 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nyamuka! Lira mofuula usiku, pa nthawi yoyamba ulonda.

      Khuthula mtima wako pamaso pa Yehova ngati madzi.

      Pemphera utakweza manja ako kwa iye chifukwa cha ana ako,

      Amene akukomoka ndi njala pamphambano za misewu yonse.+

  • Maliro 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Azimayi amene amakhala achifundo, aphika ana awo ndi manja awo.+

      Anawo akhala chakudya chawo pa nthawi yachisoni pamene mwana wamkazi wa anthu anga wawonongedwa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani