Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Oweruza 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anayamba kufunsana kuti: “Pa mafuko onse a Isiraeli ndi ndani sanabwere pamaso pa Yehova ku Mizipa?”+ Ndiyeno anaona kuti panalibe aliyense wochokera ku Yabesi-giliyadi amene anabwera kumsasa kumene kunali mpingowo.

  • 1 Samueli 31:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anthu a ku Yabesi-giliyadi+ atamva zimene Afilisiti anamuchita Sauli, 12 asilikali onse ananyamuka nʼkuyenda usiku wonse ndipo anakachotsa mtembo wa Sauli ndi mitembo ya ana ake pakhoma la mzinda wa Beti-sani. Kenako anabwerera ku Yabesi nʼkutentha mitemboyo kumeneko.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani