Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 1:39, 40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Ndiyeno wansembe Zadoki anatenga nyanga ya mafuta+ mutenti+ nʼkudzoza Solomo.+ Zitatero anthuwo anayamba kuliza lipenga nʼkumafuula kuti: “Mfumu Solomo akhale ndi moyo wautali!” 40 Atatero anthuwo anayamba kumulondola ndipo ankaimba zitoliro akusangalala kwambiri, moti nthaka inangʼambika chifukwa cha phokoso lawo.+

  • 2 Mafumu 11:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mafumu 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mbiri 12:39, 40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Anthuwa anakhala kumeneko ndi Davide masiku atatu ndipo ankadya ndi kumwa zimene abale awo anawakonzera. 40 Ndiponso anthu onse apafupi ndi kumeneko, mpaka kumadera a Isakara, Zebuloni ndi Nafitali, ankabweretsa chakudya pa abulu, ngamila, nyulu* ndi ngʼombe. Anabweretsa zakudya zophikidwa ndi ufa. Anabweretsanso makeke a nkhuyu, makeke a mphesa, vinyo, mafuta, ngʼombe ndi nkhosa. Anabweretsa zambirimbiri chifukwa anthu mu Isiraeli anasangalala kwambiri.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani