Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yoswa 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yoswa 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Zikilaga,+ Beti-marikaboti, Hazara-susa,

  • 1 Samueli 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Samueli 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Sauli atamwalira, ndiponso Davide atabwera kuchokera kokagonjetsa* Aamaleki, Davideyo anakhala ku Zikilaga+ masiku awiri.

  • 1 Mbiri 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Awa ndi anthu amene anapita kwa Davide ku Zikilaga+ pa nthawi imene iye sankayenda momasuka chifukwa choopa Sauli+ mwana wa Kisi. Iwowa anali ena mwa asilikali amphamvu amene anamuthandiza pankhondo.+

  • 1 Mbiri 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Davide atapita ku Zikilaga,+ anthu ena a fuko la Manase anapita kumbali yake. Anthuwo anali Adinala, Yozabadi, Yediyaeli, Mikayeli, Yozabadi, Elihu ndi Ziletai. Aliyense anali mtsogoleri wa asilikali 1,000, a fuko la Manase.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani