Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 29:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno akalonga a Afilisiti anafunsa kuti: “Kodi Aheberiwa akudzatani kuno?” Akisi anayankha akalonga a Afilisitiwo kuti: “Uyu ndi Davide, mtumiki wa Mfumu Sauli ya Isiraeli. Iye wakhala ndi ine kwa chaka chimodzi kapena kuposa.+ Kuyambira tsiku limene anathawira kwa ine mpaka lero, sindinamupeze ndi vuto lililonse.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani