-
2 Samueli 16:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Pa nthawiyo, malangizo a Ahitofeli+ ankaonedwa ngati mawu ochokera kwa Mulungu woona. Umu ndi mmene Davide ndi Abisalomu ankaonera malangizo onse a Ahitofeli.
-
-
Miyambo 21:30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
30 Palibe nzeru kapena kuzindikira, kapena malangizo amene angalepheretse zimene Yehova amafuna.+
-