Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako Sauli anauza womunyamulira zida kuti: “Solola lupanga lako undibaye kuti anthu osadulidwawa+ asandipeze nʼkundipha mwankhanza.” Koma womunyamulira zidayo sankafuna chifukwa ankachita mantha kwambiri. Choncho Sauli anatenga lupanga lake nʼkuligwera.+

  • 1 Mafumu 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Zimiri ataona kuti mzindawo walandidwa, anakalowa munsanja yomwe inali panyumba ya mfumu nʼkuyatsa nyumbayo iye ali momwemo, moti anafa.+

  • Salimo 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Mulungu adzawapeza ndi mlandu.

      Adzagwa chifukwa cha ziwembu zawo zomwe.+

      Muwathamangitse chifukwa cha kuchuluka kwa zolakwa zawo,

      Chifukwa iwo akupandukirani.

  • Salimo 55:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma inu Mulungu, mudzatsitsira oipawo mʼdzenje lakuya.+

      Anthu amene ali ndi mlandu wa magazi komanso achinyengowo, sadzakwanitsa kukhala ngakhale hafu ya moyo wawo.+

      Koma ine ndidzakhulupirira inu.

  • Mateyu 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Mateyu 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Machitidwe 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani