-
Deuteronomo 27:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 ‘Wotembereredwa ndi munthu wobisalira mnzake nʼkumupha.’+ (Anthu onse azidzayankha kuti, ‘Zikhale momwemo!’)
-
-
Salimo 109:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Ana ake* aziyendayenda ndipo akhale opemphapempha.
Azichoka mʼmabwinja mmene akukhala, nʼkukafunafuna chakudya.
-