Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 7:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Solomo sanayeze kulemera kwa ziwiya zonse chifukwa zinali zambiri. Kopayo sanadziwike kulemera kwake.+

  • 1 Mbiri 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Komanso Davide anasonkhanitsa zitsulo zambirimbiri zopangira misomali ya zitseko za mageti ndiponso zopangira zida zopanira zinthu. Anasonkhanitsanso kopa* wambirimbiri wosatheka kumuyeza kulemera kwake.+

  • 1 Mbiri 22:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 52:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma zinali zosatheka kuyeza kulemera kwa kopa wa zipilala ziwiri zija, thanki yosungira madzi, ngʼombe zakopa 12+ zimene zinali pansi pa thanki yosungira madzi ndiponso zotengera zokhala ndi mawilo zimene Mfumu Solomo anapanga kuti zizigwira ntchito panyumba ya Yehova chifukwa anali wochuluka kwambiri.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani