Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 28:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndipo pa nthawi imene Mfumu Ahazi ankakumana ndi mavuto, anawonjezera kuchita zosakhulupirika kwa Yehova. 23 Ahaziyo anayamba kupereka nsembe kwa milungu ya ku Damasiko+ imene inamugonjetsa,+ ndipo anati: “Milungu ya mafumu a Siriya ikuwathandiza, choncho ndipereka nsembe kwa milunguyi kuti inenso indithandize.”+ Koma milunguyo inachititsa kuti iye ndi Aisiraeli onse akumane ndi mavuto.

  • Yeremiya 44:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Nsembe zimene inuyo, makolo anu, mafumu anu, akalonga anu ndi anthu amʼdzikolo ankapereka mʼmizinda ya Yuda ndi mʼmisewu ya Yerusalemu,+ Yehova anazikumbukira ndipo zinalowa mumtima mwake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani