Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mbiri 25:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mbiri 25:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ana onsewa ankayangʼaniridwa ndi bambo awo poimba nyimbo panyumba ya Yehova. Ankaimba nyimbozo ndi zinganga, zoimbira za zingwe ndi azeze,+ potumikira panyumba ya Mulungu woona.

      Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani ankayangʼaniridwa ndi mfumu.

  • 2 Mbiri 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfumuyo inagwiritsa ntchito matabwa a mʼbawawo popanga masitepe a nyumba ya Yehova+ komanso a nyumba ya mfumu.+ Inagwiritsanso ntchito matabwawo kupanga azeze ndi zoimbira za zingwe za oimba.+ Matabwa a mʼbawa otere, sanaonekeponso mʼdziko la Yuda.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani