-
1 Mbiri 16:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Pa tsiku limeneli mʼpamene Davide kwa nthawi yoyamba anathandiza nawo kuimba nyimbo yothokoza Yehova kudzera mwa Asafu+ ndi abale ake yakuti:
-