Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mafumu 8:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Solomo anapereka nsembe zamgwirizano+ kwa Yehova. Anapereka ngʼombe 22,000 ndi nkhosa 120,000. Choncho mfumuyo ndi Aisiraeli onse anatsegulira nyumba ya Yehova.+

  • 1 Mbiri 29:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anthuwo anayamba kupereka nsembe kwa Yehova ndipo anapereka nsembe zopsereza+ kwa Yehova mpaka tsiku lotsatira. Anapereka ngʼombe zamphongo zazingʼono 1,000, nkhosa zamphongo 1,000, ana a nkhosa amphongo 1,000 ndi nsembe zake zachakumwa.+ Iwo anapereka nsembe zambirimbiri za Aisiraeli onse.+ 22 Pa tsikulo, iwo anadya ndi kumwa mosangalala kwambiri+ pamaso pa Yehova. Kachiwirinso, anaveka Solomo mwana wa Davide ufumu ndipo anamudzoza pamaso pa Yehova kukhala mtsogoleri.+ Anadzozanso Zadoki kukhala wansembe.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani