Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 24:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndi ndani angakwere kuphiri la Yehova,+

      Ndipo ndi ndani angaime mʼmalo ake opatulika?

       4 Aliyense amene ndi wosalakwa komanso wopanda chinyengo mumtima mwake,+

      Amene sanalumbire mwachinyengo potchula moyo Wanga,*

      Kapena kulumbira pofuna kupusitsa anthu ena.+

  • Salimo 84:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Osangalala ndi anthu amene amapeza mphamvu kuchokera kwa inu,+

      Amene mitima yawo imalakalaka misewu yaikulu yopita kunyumba yanu.

  • Salimo 84:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mphamvu zawo zidzapitiriza kuwonjezeka pamene akuyenda.+

      Aliyense wa iwo amaonekera pamaso pa Mulungu mu Ziyoni.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani