Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Yobu anatenga phale loti azidzikandira ndipo ankakhala paphulusa.+

  • Yobu 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako anakhala pansi limodzi ndi Yobuyo kwa masiku 7 masana ndi usiku. Palibe amene analankhula naye chilichonse chifukwa anaona kuti ululu wake unali waukulu kwambiri.+

  • Yobu 7:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndikagona ndimafunsa kuti, ‘Kodi kucha nthawi yanji?’+

      Usikuwo umatalika ndipo ndimangotembenukatembenuka mpaka mʼbandakucha.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani