Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 24:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Bambo anga, onani kansalu aka, kamʼmunsi mwa mkanjo wanu wodula manja. Pamene ndimadula kansalu kameneka sindinakupheni. Ndiye mukhoza kuona kuti ndilibe maganizo oipa kapena oukira, ndipo sindinakuchimwireni.+ Koma inuyo mukufunafuna moyo wanga kuti mundiphe.+

  • 1 Samueli 26:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Davide ananenanso kuti: “Nʼchifukwa chiyani mbuyanga mukundithamangitsa ine mtumiki wanu?+ Ndachita chiyani ine, ndipo ndalakwa chiyani?+

  • Salimo 69:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani