-
Yesaya 30:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Taonani! Dzina la Yehova likubwera kuchokera kutali.
Likubwera ndi mkwiyo wake woyaka moto ndiponso mitambo yolemera.
Iye akulankhula mwaukali,
Ndipo lilime lake lili ngati moto wowononga.+
-