-
Yeremiya 25:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Yehova Mulungu wa Isiraeli anandiuza kuti: “Tenga kapu iyi ya vinyo wa mkwiyo imene ili mʼdzanja langa ndipo ukamwetse mitundu yonse imene ndikukutumizako.
-
-
Yeremiya 25:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Ngati angakakane kulandira kapuyi mʼmanja mwako kuti amwe, ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Mukuyenera kumwa basi.
-
-
Yeremiya 49:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Yehova wanena kuti: “Taonani! Ngati amene sanapatsidwe chiweruzo kuti amwe zamʼkapu akuyenera kumwa, kodi iweyo ukuyenera kusiyidwa osapatsidwa chilango? Ayi, sudzasiyidwa osapatsidwa chilango chifukwa ukuyenera kumwa zamʼkapumo.”+
-