Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 21:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mulungu adzalanga ana a munthu woipa chifukwa cha zolakwa za bambo awo.

      Koma Mulungu amulangenso iyeyo kuti adziwe kulakwa kwake.+

      20 Maso ake aone iye akamawonongedwa,

      Ndipo adzamwe mkwiyo wa Wamphamvuyonse.+

  • Yeremiya 25:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova Mulungu wa Isiraeli anandiuza kuti: “Tenga kapu iyi ya vinyo wa mkwiyo imene ili mʼdzanja langa ndipo ukamwetse mitundu yonse imene ndikukutumizako.

  • Yeremiya 25:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ngati angakakane kulandira kapuyi mʼmanja mwako kuti amwe, ukawauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Mukuyenera kumwa basi.

  • Yeremiya 49:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova wanena kuti: “Taonani! Ngati amene sanapatsidwe chiweruzo kuti amwe zamʼkapu akuyenera kumwa, kodi iweyo ukuyenera kusiyidwa osapatsidwa chilango? Ayi, sudzasiyidwa osapatsidwa chilango chifukwa ukuyenera kumwa zamʼkapumo.”+

  • Chivumbulutso 14:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Chivumbulutso 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Chivumbulutso 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani