Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mbiri 16:23-25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Dziko lonse lapansi liimbire Yehova!

      Tsiku ndi tsiku muzilengeza za chipulumutso chake!+

      24 Lengezani ulemerero wake pakati pa anthu a mitundu ina,

      Lengezani ntchito zake zodabwitsa pakati pa mitundu yonse ya anthu.

      25 Chifukwa Yehova ndi wamkulu komanso woyenera kutamandidwa,

      Iye ndi wochititsa mantha kwambiri kuposa milungu ina yonse.+

  • Salimo 66:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani