Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 7:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 musawaope.+ Nthawi zonse muzikumbukira zimene Yehova Mulungu wanu anachitira Farao ndi Iguputo yense.+ 19 Muzikumbukira ziweruzo zamphamvu zimene* maso anu anaona, zizindikiro, zodabwitsa,+ dzanja lamphamvu ndiponso mkono wotambasula umene Yehova Mulungu wanu anagwiritsa ntchito pokutulutsani mʼdzikolo.+ Izi ndi zimene Yehova Mulungu wanu adzachite ndi anthu a mitundu yonse amene mukuwaopa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani