Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Genesis 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Genesis 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mbiri 16:19-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamene ankanena zimenezi nʼkuti inu mulipo ochepa,

      Nʼkuti mulipo ochepa kwambiri komanso muli alendo mʼdzikolo.+

      20 Iwo ankayendayenda kuchokera ku mtundu wina kupita ku mtundu wina,

      Komanso kuchokera mu ufumu wina kupita kwa anthu a mtundu wina.+

      21 Mulungu sanalole kuti munthu aliyense awapondereze,+

      Koma anadzudzula mafumu chifukwa cha iwo.+

      22 Iye anati: ‘Musakhudze odzozedwa anga,

      Ndipo aneneri anga musawachitire choipa chilichonse.’+

  • Machitidwe 7:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani