-
Danieli 9:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Ife tachimwa, tachita zinthu zolakwika komanso zoipa ndipo takupandukirani.+ Tapatuka nʼkusiya kutsatira malamulo ndi zigamulo zanu.
-