Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 43:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Usachite mantha chifukwa ine ndili ndi iwe.+

      Ndidzabweretsa mbadwa* zako kuchokera kumʼmawa,

      Ndipo ndidzakusonkhanitsani pamodzi kuchokera kumadzulo.+

       6 Ndidzauza kumpoto kuti, ‘Abwezere kwawo!’+

      Ndipo ndidzauza kumʼmwera kuti, ‘Usawakanize.

      Bweretsa ana anga aamuna kuchokera kutali komanso ana anga aakazi kuchokera kumalekezero a dziko lapansi.+

  • Yeremiya 31:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ine ndikuwabweretsa kuchokera kudziko lakumpoto,+

      Ndidzawasonkhanitsa pamodzi kuchokera kumalekezero a dziko lapansi.+

      Pakati pawo padzakhala anthu amene ali ndi vuto losaona, olumala,+

      Azimayi oyembekezera komanso amene atsala pangʼono kubereka,

      Onse pamodzi adzabwerera kuno ali chigulu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani