Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 15:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Komanso pamene Abisalomu ankapereka nsembe, anaitanitsa Ahitofeli+ wa ku Gilo, mlangizi wa Davide,+ kuchoka kumzinda wakwawo wa Gilo.+ Anthu amene anagwirizana ndi Abisalomu pa chiwembuchi anapitiriza kuwonjezeka.+

  • 2 Samueli 16:5-7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mfumu Davide itafika ku Bahurimu, mwamuna wina wa mʼbanja la Sauli, dzina lake Simeyi,+ mwana wa Gera anatulukira akulankhula mawu onyoza.+ 6 Iye anayamba kugenda Davide, atumiki onse a Mfumu Davide, anthu onse komanso amuna onse amphamvu amene anali kumanja ndi kumanzere kwa mfumu. 7 Simeyi ankanena kuti: “Choka! Choka! Munthu wa mlandu wa magazi ndiponso wopanda pake iwe!

  • Salimo 69:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani