Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 35:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mboni zoipa mtima zabwera,+

      Ndipo zikundifunsa zinthu zimene sindikuzidziwa.

      12 Iwo amandibwezera zoipa mʼmalo mwa zabwino,+

      Ndipo ndimakhala wachisoni ngati namfedwa.

  • Salimo 38:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma adani anga ndi amphamvu kwambiri,

      Ndipo odana nane popanda chifukwa anachuluka.

      20 Iwo anandibwezera choipa mʼmalo mwa chabwino,

      Ndikafuna kuchita zabwino iwo ankandiletsa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani