Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 18:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Inu mumandipatsa chishango chanu chachipulumutso,+

      Dzanja lanu lamanja limandithandiza,*

      Ndipo kudzichepetsa kwanu nʼkumene kumandikweza.+

  • Salimo 138:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 57:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 66:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Dzanja langa ndi limene linapanga zinthu zonsezi,

      Ndipo izi ndi zimene zinachitika kuti zonsezi zikhalepo,” akutero Yehova.+

      “Choncho ine ndidzayangʼana munthu ameneyu,

      Ndidzayangʼana munthu wodzichepetsa ndiponso wosweka mtima amene amadera nkhawa mawu anga.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani