Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 77:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndikuganizira masiku akale,+

      Ndikuganizira zaka zakale kwambiri.

       6 Usiku ndimakumbukira nyimbo yanga.*+

      Ndimaganiza mumtima mwanga,+

      Ndipo ndimafufuza mwakhama.

  • Salimo 77:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 111:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ntchito za Yehova ndi zazikulu,+

      ד [Daleth]

      Anthu onse amene amasangalala nazo amaziphunzira.+

      ה [He]

       3 Zochita zake zimasonyeza ulemerero ndi ulemu,

      ו [Waw]

      Ndipo chilungamo chake chidzakhalapobe kwamuyaya.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani