Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 49:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Aliyense amaona kuti ngakhale anthu anzeru amafa,

      Munthu wopusa komanso munthu wopanda nzeru, onse amawonongeka,+

      Ndipo chuma chawo amasiyira anthu ena.+

  • Mlaliki 2:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndinayamba kudana ndi zinthu zonse zimene ndinapeza nditagwira ntchito mwakhama padziko lapansi pano,+ chifukwa ndidzayenera kusiyira munthu amene akubwera pambuyo panga.+ 19 Ndipo ndi ndani akudziwa ngati angadzakhale wanzeru kapena wopusa?+ Koma adzatenga zinthu zanga zonse zimene ndinapeza nditagwira ntchito mwakhama komanso mwanzeru padziko lapansi pano. Zimenezinso nʼzachabechabe.

  • Mlaliki 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pali munthu amene ali yekhayekha, wopanda mnzake. Alibe mwana kapena mchimwene wake, koma amangokhalira kugwira ntchito mwakhama. Maso ake sakhutira ndi chuma.+ Koma kodi amadzifunsa kuti, “Ndikamagwira ntchito mwakhama komanso kudzimana zinthu zabwino, kodi ndikufuna kuti zinthu zimenezi adzasangalale nazo ndani?”+ Izinso nʼzachabechabe ndipo ndi ntchito yobweretsa nkhawa.+

  • Luka 12:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani