Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Miyambo 30:21-23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pali zinthu zitatu zimene zimagwedeza dziko lapansi

      Ndiponso zinthu 4 zimene dziko lapansi silitha kuzipirira. Zinthu zake ndi izi:

      22 Kapolo akamalamulira monga mfumu,+

      Munthu wopusa akamadya kwambiri,

      23 Mkazi amene amadedwa* akakwatiwa,

      Komanso mtsikana wantchito akatenga malo a abwana ake aakazi.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani