Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 64:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndibiseni ku ziwembu zachinsinsi za anthu oipa,+

      Kwa gulu la anthu ochita zoipa.

  • Salimo 64:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Adzawonongedwa chifukwa cha zolankhula za lilime lawo lomwe,+

      Onse amene adzaone zimenezi adzapukusa mitu yawo.

  • Miyambo 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anzeru ndi amene amapitiriza kuphunzira zinthu zamtengo wapatali,+

      Koma pakamwa pa wopusa pamachititsa kuti awonongedwe.+

  • Miyambo 10:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Milomo ya wolungama imathandiza* anthu ambiri,+

      Koma zitsiru zimafa chifukwa chopanda nzeru.+

  • Miyambo 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani