Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Miyambo 5:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kasupe wako akhale wodalitsidwa,*

      Ndipo uzisangalala ndi mkazi amene unamukwatira udakali wachinyamata.+

      19 Iye akhale ngati mbawala yaikazi yachikondi komanso ngati kamwana ka mbuzi zamʼmapiri kokongola.+

      Mabere ake azikukhutiritsa* nthawi zonse.

      Chikondi chake chizikusangalatsa kwambiri nthawi zonse.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani