Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nyimbo ya Solomo 4:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Ndiwe wokongola wokondedwa wanga.

      Ndiwe chiphadzuwa.

      Maso ako ali ngati maso a njiwa munsalu yako yophimba kumutuyo.

      Tsitsi lako lili ngati gulu la mbuzi

      Zimene zikuthamanga potsika mapiri a ku Giliyadi.+

       2 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zomwe angozimeta kumene,

      Zimene zikuchokera kosambitsidwa,

      Zonse zabereka mapasa,

      Ndipo palibe imene ana ake afa.

       3 Milomo yako ili ngati chingwe chofiira kwambiri,

      Ndipo ukamalankhula umasangalatsa.

      Masaya ako munsalu yako yophimba kumutuyo

      Ali ngati khangaza* logamphula pakati.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani