Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 30:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Ekisodo 30:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Esitere 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mtsikana aliyense ankakhala ndi nthawi yake yokaonekera kwa Mfumu Ahasiwero akamaliza kumuchitira zonse zimene amayenera kuwachitira akazi pa miyezi 12. Atsikanawo ankawapaka mafuta a mule*+ miyezi 6 kenako nʼkuwapakanso mafuta a basamu+ pamodzi ndi mafuta enanso okongoletsa miyezi inanso 6. Akachita zimenezi ankakhala kuti amaliza dongosolo lonse lowakongoletsera.

  • Salimo 45:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nyimbo ya Solomo 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 “Mpaka kunja kutayamba kuwomba kamphepo kayaziyazi ndiponso mpaka mithunzi itachoka,

      Ndipita kuphiri la mule

      Ndiponso kuzitunda za lubani.”+

  • Nyimbo ya Solomo 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Masaya ake ali ngati bedi la maluwa onunkhira,+

      Ndiponso ngati munda wa zitsamba zonunkhira umene uli pamalo okwera.

      Milomo yake ili ngati maluwa amene akuchucha mafuta a mule.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani