-
Mika 2:1, 2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 “Tsoka kwa anthu amene amakonza chiwembu,
Amene akagona pabedi pawo, amaganizira kuti achite zoipa.
Ndipo mʼmawa kukacha, amazichitadi.
Chifukwa ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.+
-