Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Mika 2:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Tsoka kwa anthu amene amakonza chiwembu,

      Amene akagona pabedi pawo, amaganizira kuti achite zoipa.

      Ndipo mʼmawa kukacha, amazichitadi.

      Chifukwa ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.+

       2 Iwo amalakalaka minda ya anthu ena ndipo amaitenga.+

      Amalakalakanso nyumba za anthu ena nʼkuzitenga.

      Amatenga mwachinyengo nyumba ya munthu,+

      Ndipo amatenganso cholowa cha munthu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani