-
Deuteronomo 28:63Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
63 Mofanana ndi mmene Yehova anasangalalira kuchititsa kuti zinthu zikuyendereni bwino komanso kuchititsa kuti muchuluke, Yehova adzasangalalanso kuti akuwonongeni nʼkukufafanizani, ndipo mudzatheratu mʼdziko limene mukupita kukalitenga kuti likhale lanu.
-
-
Ezekieli 24:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 ‘Uza nyumba ya Isiraeli kuti: “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ndatsala pangʼono kudetsa malo anga opatulika,+ chinthu chimene mumachinyadira kwambiri, chinthu chimene mumachikonda komanso chapamtima panu. Ana anu aamuna ndi aakazi amene munawasiya mumzindawo adzaphedwa ndi lupanga.+
-