Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 49:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mafumu adzakhala okusamalira,+

      Ndipo ana awo aakazi adzakhala okuyamwitsira ana ako.

      Iwo adzakugwadira mpaka nkhope zawo pansi+

      Ndipo adzanyambita fumbi lakumapazi ako.+

      Choncho iwe udzadziwa kuti ine ndine Yehova.

      Anthu amene amandikhulupirira sadzachita manyazi.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani