Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 16:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Ahazi anatenga siliva ndi golide wapanyumba ya Yehova ndiponso wochokera mʼnyumba ya mfumu nʼkutumiza kwa mfumu ya Asuri ngati chiphuphu.+ 9 Mfumu ya Asuri inamvera pempho lake ndipo inapita ku Damasiko nʼkukalanda mzindawo. Anthu amumzindawo inawagwira nʼkupita nawo ku Kiri+ ndipo Rezini inamupha.+

  • Yesaya 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 chifukwa mwanayo asanadziwe kuitana kuti, ‘Ababa!’ kapena ‘Amama!’ chuma cha ku Damasiko ndi katundu wolandidwa ku Samariya zidzatengedwa nʼkupita nazo kwa mfumu ya Asuri.”+

  • Amosi 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndidzathyola mipiringidzo ya mageti a Damasiko.+

      Ndidzapha anthu a ku Bikati-aveni,

      Komanso wolamulira* ku Beti-edeni.

      Ndipo anthu a ku Siriya adzapita ku ukapolo ku Kiri,”+ watero Yehova.’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani