-
Yesaya 1:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Yehova wanena kuti: “Kodi nsembe zanu zambirimbirizo zili ndi phindu lanji kwa ine?+
-
-
Yeremiya 15:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Kenako Yehova anandiuza kuti: “Ngakhale Mose ndi Samueli akanaima pamaso panga,+ anthu awa sindikanawakomera mtima. Achotse pamaso panga. Asiye apite.
-