Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 9:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 “Aliyense asamale ndi mnzake,

      Ndipo musamakhulupirire ngakhale mʼbale wanu.

      Chifukwa munthu aliyense ndi wachinyengo,+

      Ndipo munthu aliyense akunenera mnzake zoipa.+

       5 Aliyense amapusitsa mnzake,

      Ndipo palibe amene amalankhula zoona.

      Aphunzitsa lilime lawo kulankhula chinyengo.+

      Iwo amadzitopetsa okha pochita zinthu zoipa.

  • Mika 3:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma mumadana ndi zinthu zabwino+ ndipo mumakonda zinthu zoipa.+

      Mumasenda khungu la anthu anga nʼkuchotsa mnofu pamafupa awo.+

       3 Mumadyanso mnofu wa anthu anga,+

      Ndipo mumasenda khungu lawo.

      Mumaswa mafupa awo nʼkuwaphwanyaphwanya.+

      Ngati zinthu zimene zaphikidwa mumphika* komanso ngati nyama imene ili mumphika.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani