Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 20:16-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno Yesaya anauza Hezekiya kuti: “Imva zimene Yehova wanena,+ 17 ‘Masiku akubwera pamene zinthu zonse zimene zili mʼnyumba mwako ndiponso zonse zimene makolo ako akhala akusunga mpaka lero, anthu adzazitenga nʼkupita nazo ku Babulo.+ Palibe chidzatsale,’ watero Yehova. 18 ‘Ena mwa ana ako, amene iweyo udzabereke, adzatengedwa+ ndipo adzakhala nduna zapanyumba ya mfumu ya ku Babulo.’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani