Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nehemiya 3:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Palali mwana wa Uzai, anakonza mpandawo kutsogolo kwa khoma lothandizira kuti mpanda usagwe. Anakonzanso nsanja yochokera pa Nyumba ya Mfumu+ imene ili kumtunda mʼBwalo la Alonda.+ Pedaya mwana wa Parosi, anapitiriza kuchokera pamene Palali+ analekezera.

  • Yeremiya 32:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pa nthawi imeneyo, asilikali a mfumu ya Babulo anali atazungulira Yerusalemu. Ndipo mneneri Yeremiya anali atamutsekera mʼnyumba imene inali mʼBwalo la Alonda,+ limene linali pafupi ndi nyumba ya mfumu ya Yuda.

  • Yeremiya 33:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Yeremiya adakali mʼBwalo la Alonda+ momwe anamutsekera, Yehova analankhula naye kachiwiri kuti:

  • Yeremiya 38:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 ndipo iwo anakoka Yeremiya ndi zingwezo nʼkumutulutsa mʼchitsimemo. Yeremiya anapitiriza kukhala mʼBwalo la Alonda.+

  • Yeremiya 38:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Yeremiya anapitirizabe kukhala mʼBwalo la Alonda+ mpaka tsiku limene Yerusalemu analandidwa. Iye anali adakali konko pamene Yerusalemu analandidwa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani