Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 25:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mʼchaka cha 9 cha ufumu wa Zedekiya, mʼmwezi wa 10, pa tsiku la 10 la mweziwo, Nebukadinezara+ mfumu ya Babulo anabwera ku Yerusalemu pamodzi ndi asilikali ake onse.+ Anabwera kudzamenyana ndi anthu amumzindawo ndipo anamanga msasa komanso mpanda kuzungulira mzinda wonsewo.+ 2 Mzindawo unazunguliridwa mpaka chaka cha 11 cha Mfumu Zedekiya.

  • Yeremiya 52:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mʼchaka cha 9 cha ufumu wa Zedekiya, mʼmwezi wa 10, pa tsiku la 10 la mweziwo, Nebukadinezara* mfumu ya Babulo anabwera ku Yerusalemu pamodzi ndi asilikali ake onse. Anabwera kudzamenyana ndi anthu amumzindawo ndipo anamanga msasa komanso mpanda kuzungulira mzinda wonsewo.+ 5 Mzindawo unazunguliridwa mpaka chaka cha 11 cha Mfumu Zedekiya.

  • Ezekieli 24:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Yehova analankhulanso nane mʼchaka cha 9, mʼmwezi wa 10, pa tsiku la 10 la mweziwo, kuti: 2 “Iwe mwana wa munthu, lemba deti lalero,* ulembe tsiku lalero. Lero mfumu ya Babulo yayamba kuukira mzinda wa Yerusalemu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani